Ndiwe Wanga


Verse; 1
Pazachikondi chako dziwa ine ndi mboni
Sindinalakelake kupita ku Joni
Chikondi cha iwe ndi ine sicham'mafoni
Nchifukwa sindinapite ku bank kukatenga loan
Chikondi chathu chobeba chanoninoni
Umandizula moyo ukapereka moni
Umandikumbutsa za kwathu kumangoni
Ndakondwa umadziwa kuti ine ndi m'goni

Chorus*2
Ndiwe wanga ndiwe kuwala kwanga
Ndiwe wanga ndiwe nyenyezi yanga
Ndiwe wanga ndiwe wanga ndiwe wapamtima wanga
Ndiwe wanga ndiwe wanga nyenyezi yanga
Ndiwe wanga ndiwe kuwala kwanga

Verse; 2
Ndikakha pansi ndimadziwa ndiri ndi mzanga
Kuyenda limodzi tifanana mawanga
Amandinena ati ndiri nyanga
Asatilongoze monga ichita nkhanga
Ndithudi ndilonjeza ndzakutengela kunyanja
Nthawi imeneyo tikukonzekera banja
Ona ambiri akutiombera m'manja
Mpakana wena kutimangira nsanja

(Back to chorus)

Verse; 3
Chikondi chathu chansangala sizachisoni
Ena amasangalala akatipatsa moni
Unasiya amabenzi onse ndimalinkoni
Amatithila madzi ndikumaimba horn
Akamadutsa baby, Samamvetsa baby
Ngati andale baby, Ali pa njale baby
Zimawawawa baby, Kuiwala mawa baby
Ngati moyenda baby, Ife tikuyenda baby!, Hee!

(Back to chorus till the end)







Captcha
Widget
The Maskal Ndiwe Wanga are brought to you by Lyrics-Keeper. You can use lyrics widget for karaoke. We tried to make lyrics as correct as possible, however if you have any corrections for Ndiwe Wanga lyrics, please feel free to submit them to us. If you want to download this song in mp3 you can visit one of our music sponsors.