Текст песни National Anthem: Malawi Native Anthem Text

Malawi Native Anthem Text


Mlungu dalitsani Malawi,
Mumsunge m'mtendere
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje
Lunzitsani mitima yathu,
Kuti tisaope
Mdalitse Mtsogo leri na fe,
Ndi Mai Malawi

Malawi ndziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,
Ndithudi tadala
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
N'mphatso zaulere
Nkhalango, madambo abwino
Ngwokoma Malawi

O! Ufulu tigwirizane,
Kukweza Malawi
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire
Pa nkhondo nkana pa mtendere,
Cholinga n'chimodzi
Mai, bambo, tidzipereke,
Pokweza Malawi
Sent by Carlos André Pereira da Silva Branco







Captcha
Песня National Anthem Malawi Native Anthem Text представлена вам Lyrics-Keeper. Виджет можно использовать в качестве караоке к песне Malawi Native Anthem Text, если есть возможность скачать минусовку. Для некоторых композиций доступен правильный перевод песни. Мы стараемся сделать так, чтобы слова песни Malawi Native Anthem Text были наиболее точными, поэтому если у вас есть какие-то корректировки текста, пожалуйста отправляйте их нам. Если вы хотите скачать бесплатно эту песню в формате mp3, посетите одного из наших музыкальных спонсоров.